-
Kukonzekera Kuyang’anizana ndi ChizunzoNsanja ya Olonda—1987
-
-
“Ndipo,“ Yesu akupitiriza, “mbale adzapereka mbale wake ku imfa, ndi atate mwana wake, ndipo ana adzatsutsa akuwabala, nadzawafetsa iwo.” lye akuwonjezera: “Ndipo adzada inu anthu onse chifukwa cha dzina langa; koma iye wakupirira kufikira chimariziro, iyeyu adzapulumutsidwa.”
-
-
Kukonzekera Kuyang’anizana ndi ChizunzoNsanja ya Olonda—1987
-
-
Chiri chowona kuti Yesu anapereka malangizo awa, chenjezo, ndi chilimbikitso kwa atumwi ake 12, koma chinatanthauzidwanso kaamba ka awo omwe adzagawanamo mu kulalikira kwa dziko lonse pambuyo pa imfa yake ndi chiukiriro. Ichi chikusonyezedwa ndi chenicheni chakuti iye ananena kuti ophunzira ake ‘adzadedwa ndi anthu onse, ’osati kokha ndi Aisrayeli kwa amene atumwiwo anatumizidwa kukalalikira. Kuwonjezerapo, atumwiwo mwachiwonekere sanaperekedwe pamaso pa olamulira ndi mafumu pamene Yesu anawatumiza iwo ku ndawala zawo zazifupi zolalikira. Ndiponso, okhulupirirawo sanaperekedwe ku imfa ndi ziwalo zabanja.
-