Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Kukonzekera Kuyang’anizana ndi Chizunzo
    Nsanja ya Olonda—1987
    • “Ndipo,“ Yesu akupitiriza, “mbale adzapereka mbale wake ku imfa, ndi atate mwana wake, ndipo ana adzatsutsa akuwabala, nadzawafetsa iwo.” lye akuwonjezera: “Ndipo adzada inu anthu onse chifukwa cha dzina langa; koma iye wakupirira kufikira chimariziro, iyeyu adzapulumutsidwa.”

  • Kukonzekera Kuyang’anizana ndi Chizunzo
    Nsanja ya Olonda—1987
    • Chiri chowona kuti Yesu anapereka malangizo awa, chenjezo, ndi chilimbikitso kwa atumwi ake 12, koma chinatanthauzidwanso kaamba ka awo omwe adzagawanamo mu kulalikira kwa dziko lonse pambuyo pa imfa yake ndi chiukiriro. Ichi chikusonyezedwa ndi chenicheni chakuti iye ananena kuti ophunzira ake ‘adzadedwa ndi anthu onse, ’osati kokha ndi Aisrayeli kwa amene atumwiwo anatumizidwa kukalalikira. Kuwonjezerapo, atumwiwo mwachiwonekere sanaperekedwe pamaso pa olamulira ndi mafumu pamene Yesu anawatumiza iwo ku ndawala zawo zazifupi zolalikira. Ndiponso, okhulupirirawo sanaperekedwe ku imfa ndi ziwalo zabanja.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena