Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Asangalatsidwa ndi Mfarisi Wotchuka
    Nsanja ya Olonda—1988 | December 15
    • “Munthu wina anakonza phwando lalikulu, naitana anthu ambiri. Ndipo anatumiza kapolo wake . . . kukanena kwa oitanidwawo, ‘Idzani, chifukwa zonse zakonzeka tsopano.’ Ndipo onse ndi mtima umodzi anayamba kuwiringula. Woyamba anati kwa iye, ‘Ine ndagula munda ndipo ndiyenera ndituluke kukawuwona; ndikupempha, Undilole ine ndisafika.’ Ndipo anati wina, ‘Ine ndagula ng’ombe za magoli asanu, ndipo ndinka kukaziyesa; ndikupempha, Undilole ine ndisafika.’ Ndipo anati wina, ‘Ine ndakwatira mkazi, ndipo chifukwa chake sindingathe kudza.’”

  • Asangalatsidwa ndi Mfarisi Wotchuka
    Nsanja ya Olonda—1988 | December 15
    • Ndi mkhalidwe wotani umene ukulongosoledwa ndi fanizoli? Chabwino, “mbuye” wopereka chakudyayo akuimira Yehova Mulungu; “kapolo” wopereka chiitanoyo, Yesu Kristu; ndipo “phwando lamadzulo,” mwaŵi wa kukhala mu mzere kaamba ka Ufumu wa kumwamba.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena