Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Kusangalala ndi Unansi Wathithithi
    Nsanja ya Olonda—1990 | August 15
    • “Ine ndine mpesa weniweni, ndipo Atate wanga ndiye wam’munda,” iye akuyamba. Wolima Wamkulu, Yehova Mulungu, anadzala mpesa wophiphiritsira umenewu pamene anamudzoza Yesu ndi mzimu woyera pa ubatizo wake m’chilimwe cha 29 C.E. Koma Yesu akupitiriza kusonyeza kuti mpesawo ukuphiphiritsira zinanso osati iye yekha, akumalongosola kuti:

      ‘Nthambi iriyonse ya mwa ine yosabala chipatso, aichotsa; ndi iriyonse yakubala chipatso, aisadza, kuti ikabale chipatso chochuluka. . . . Monga nthambi siingathe kubala chipatso pa yokha, ngati siikhala mwampesa; motere mulibe inunso ngati simukhala mwa ine. Ine ndine mpesa, inu ndinu nthambi zake.’

  • Kusangalala ndi Unansi Wathithithi
    Nsanja ya Olonda—1990 | August 15
    • Pa Pentekoste, masiku 51 pambuyo pake, atumwiwo ndi ena akukhala nthambi za mpesa pamene mzimu woyera watsanuliridwa pa iwo. Potsirizira pake, anthu 144,000 akukhala nthambi zophiphiritsira za mtengo wa mpesa. Limodzi ndi tsinde la mpesawo, Yesu Kristu, iwo akupanga mpesa wophiphiritsira umene ukubala zipatso za Ufumu wa Mulungu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena