Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Akazi Achikristu—Kusunga Umphumphu Mmalo Antchito
    Nsanja ya Olonda—1987
    • Mkazi wolingalira wotchedwa Betty amatenga chinjirizo lina lake. Iye akuti: “Ndimakhala wochenjera ponena za kuyanjana ndi anzanga ogwira nawo ntchito chifukwa makhalidwe awo siali ofanana ndi anga.” (1 Akorinto 15:33) Ichi sichikutanthauza kuti muyenera kudzipatula kapena kukhala waukali kwa ogwira nawo ntchito. Koma pamene iwo akakamira pa kukambitsirana nkhani zomwe ziri zonyansa kwa Mkristu, musachedwe kudzichotsapo inu eni. (Aefeso 5:3, 4) Kumvetsera kwanu ku nkhani yoipa imeneyo kungapereke kwa amuna apantchito chikhutiritso chakuti mungakhale wovomereza ku kukufikirani kwawo.

  • Akazi Achikristu—Kusunga Umphumphu Mmalo Antchito
    Nsanja ya Olonda—1987
    • Pomalizira, mkazi wolingalira amapewa mkhalidwe yogonjera. Kuitanidwa kumwa chakumwa choledzeretsa kapena kutsalira kuntchito pambuyo pa nthaŵi ya ntchito popanda chifukwa chenicheni kungakhale msampha. (Yerekezani ndi 2 Samueli 13:1-14. ) “Wochenjera awona zoipa nabisala,” umatero mwambo wanzeru.​—Miyambo 22:3.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena