Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • “Ali ndi Mtima Wanzeru” Koma Ndi Wodzichepetsa
    Yandikirani Yehova
    • 7 Komabe, Yehova ndi wodzichepetsa ndiponso wofatsa. Amaphunzitsa atumiki ake kuti kukhala wofatsa n’kofunika kwambiri kuti munthu akhale ndi nzeru zenizeni. Mawu ake amanena kuti ‘kufatsa ndi khalidwe limene limabwera chifukwa cha nzeru.’ (Yakobo 3:13) Taganizirani chitsanzo cha Yehova pa nkhaniyi.

  • “Ali ndi Mtima Wanzeru” Koma Ndi Wodzichepetsa
    Yandikirani Yehova
    • b N’zochititsa chidwi kuti Baibulo limanena kuti munthu wosaleza mtima amakhala wodzikuza. (Mlaliki 7:8) Choncho mfundo yoti Yehova ndi woleza mtima, ikusonyezanso kuti ndi wodzichepetsa.​—2 Petulo 3:9.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena