-
“Ali ndi Mtima Wanzeru” Koma Ndi WodzichepetsaYandikirani Yehova
-
-
7 Komabe, Yehova ndi wodzichepetsa ndiponso wofatsa. Amaphunzitsa atumiki ake kuti kukhala wofatsa n’kofunika kwambiri kuti munthu akhale ndi nzeru zenizeni. Mawu ake amanena kuti ‘kufatsa ndi khalidwe limene limabwera chifukwa cha nzeru.’ (Yakobo 3:13) Taganizirani chitsanzo cha Yehova pa nkhaniyi.
-
-
“Ali ndi Mtima Wanzeru” Koma Ndi WodzichepetsaYandikirani Yehova
-
-
b N’zochititsa chidwi kuti Baibulo limanena kuti munthu wosaleza mtima amakhala wodzikuza. (Mlaliki 7:8) Choncho mfundo yoti Yehova ndi woleza mtima, ikusonyezanso kuti ndi wodzichepetsa.—2 Petulo 3:9.
-