Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Zipembedzo Zonyenga Zimaphunzitsa Zabodza Zokhudza Mulungu
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
    • Zipembedzo zonyenga zakhala ‘zikusinthanitsa choonadi cha Mulungu ndi bodza.’ (Aroma 1:25) Mwachitsanzo, zipembedzo zambiri sizimaphunzitsa anthu dzina la Mulungu. Komatu Baibulo limaphunzitsa kuti tiyenera kugwiritsa ntchito dzina la Mulungu. (Aroma 10:13, 14) Atsogoleri ena azipembedzo amanena kuti chinachake choipa chikachitika, chimakhala kuti ndi cholinga cha Mulungu. Koma limeneli ndi bodza. Mulungu si amene amachititsa zinthu zoipa. (Werengani Yakobo 1:13.) N’zomvetsa chisoni kuti mabodza amene zipembedzozi zimaphunzitsa amachititsa kuti anthu asamakonde Mulungu.

  • N’chifukwa Chiyani Anthu Amavutika?
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
    • 4. Ndi ndani amene amachititsa kuti tizivutika?

      Anthu ambiri amakhulupilira kuti Mulungu ndi amene akulamulira dzikoli. Kodi zimenezi ndi zoona? Onerani VIDIYO.

      VIDIYO: Ndi Ndani Amene Akulamulira Dziko? (1:24)

      Werengani Yakobo 1:13 ndi 1 Yohane 5:19, kenako mukambirane funso ili:

      • Kodi Mulungu ndi amene amachititsa kuti tizivutika?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena