Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Kodi Baibulo Limanena Zotani pa Nkhani ya Ngozi Zadzidzidzi?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
    • 1 Petulo 5:6, 7: “Dzichepetseni pansi pa dzanja lamphamvu la Mulungu . . . pamene mukumutulira nkhawa zanu zonse, pakuti amakuderani nkhawa.”

      Mfundo yake: Mulungu amakhudzidwa ndi zimene zikutichitikira ndipo amafuna kuti tizimufotokozera nkhawa zathu.

  • Kodi Baibulo Lingandithandize Ngati Ndili ndi Maganizo Ofuna Kudzipha?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
      • Zimene Baibulo limanena: ‘Mutulireni [Mulungu] nkhawa zanu zonse, pakuti amakuderani nkhawa.’—1 Petulo 5:7.

        Mfundo yake: Mulungu akukupemphani kuti muzimasuka kumuuza chilichonse chimene chikukudetsani nkhawa.

        Mulungu akhoza kukupatsani mtendere wa mumtima komanso mphamvu kuti muthe kupirira mavuto amene mukukumana nawo. (Afilipi 4:6, 7, 13) Mulungu amagwiritsa ntchito njira imeneyi pothandiza anthu omwe akumupempha kuti awathandize.—Salimo 55:22.

        Munthu amene akulimbana ndi maganizo ofuna kudzipha wakhala pabenchi, wanyamula Baibulo, ndipo akuganizira zomwe wawerenga
  • Kodi M’Baibulo Mungapezeke Mawu Omwe Angandilimbikitse?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
    • 1 Petulo 5:7: ‘Mutulireni nkhawa zanu zonse, pakuti amakuderani nkhawa.’

      Mfundo yake: Mulungu amatidera nkhawa tikamavutika. Iye amatilimbikitsa kuti tizipemphera kwa iye n’kumuuza zomwe zikutidetsa nkhawa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena