Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mafunso Ochokera kwa Owerenga
    Nsanja ya Olonda—2015 | May 15
    • Nanga kodi “Gogi ndi Magogi” otchulidwa pa Chivumbulutso 20:8 ndi ndani? Zaka 1,000 zikadzatha, anthu amene adzasiye kutumikira Yehova adzakhalanso ndi mtima wachiwembu ngati wa “Gogi wa kudziko la Magogi.” Ndiye paja tanena kale kuti Gogi wa kudziko la Magogi ndi mitundu ya anthu imene idzaukire anthu a Mulungu chakumapeto kwa chisautso chachikulu. Ndiyeno zimene zidzachitikire “Gogi wa kudziko la Magogi” zidzafanana ndi zimene zidzachitikire “Gogi ndi Magogi.” Onse adzawonongedwa ndipo sadzakhalakonso. (Chiv. 19:20, 21; 20:9) Malinga ndi zimene tanenazi, “Gogi ndi Magogi” akuimira anthu onse amene adzasiye kutumikira Mulungu pambuyo pa zaka 1,000.

      Tchati chosonyeza zimene zidzachitike pambuyo pa zaka 1000
  • Mafunso Ochokera kwa Owerenga
    Nsanja ya Olonda—2015 | May 15
Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena