-
Chikristu Chifalikira Kumayiko Ena‘Onani Dziko Lokoma’
-
-
[Bokosi patsamba 33]
MIPINGO ISANU NDI IŴIRI
Yesu anatumiza uthenga ku mipingo isanu ndi iŵiri ku Asiya Mina. Onani malo amene mipingoyo inali: kunyanja ku Efeso ndi Smurna; kumtunda ku Pergamo, Filadelfeya, ndi Laodikaya; Tiyatira umene unali m’mphepete mwa mtsinje; ndi Sarde umene unali panjira yamalonda. Zotsalira za mizinda imeneyi zimene zafukulidwa zimasonyeza kuti Baibulo limanena za malo enieni.
-
-
Chikristu Chifalikira Kumayiko Ena‘Onani Dziko Lokoma’
-
-
[Mipingo isanu ndi iŵiri]
E2 Pergamo
E2 Tiyatira
E2 Sarde
E2 Smurna
E2 Efeso
F2 Filadelfeya
F2 Laodikaya
-