Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Chikristu Chifalikira Kumayiko Ena
    ‘Onani Dziko Lokoma’
    • [Bokosi patsamba 33]

      MIPINGO ISANU NDI IŴIRI

      Yesu anatumiza uthenga ku mipingo isanu ndi iŵiri ku Asiya Mina. Onani malo amene mipingoyo inali: kunyanja ku Efeso ndi Smurna; kumtunda ku Pergamo, Filadelfeya, ndi Laodikaya; Tiyatira umene unali m’mphepete mwa mtsinje; ndi Sarde umene unali panjira yamalonda. Zotsalira za mizinda imeneyi zimene zafukulidwa zimasonyeza kuti Baibulo limanena za malo enieni.

  • Chikristu Chifalikira Kumayiko Ena
    ‘Onani Dziko Lokoma’
    • [Mipingo isanu ndi iŵiri]

      E2 Pergamo

      E2 Tiyatira

      E2 Sarde

      E2 Smurna

      E2 Efeso

      F2 Filadelfeya

      F2 Laodikaya

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena