Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 9/06 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2006
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Ndingafotokoze Bwanji Zimene Ndimakhulupirira Zokhudza Chilengedwe?
    Galamukani!—2006
  • ZIMENE ACHINYAMATA AMADZIFUNSA-Kodi Zinthu Zinachita Kulengedwa?—Gawo 2
    Zimene Achinyamata Amafunsa
  • Kodi N’zoona Kuti Zamoyo Zinachokera ku Zinthu Zina?
    Mayankho a Mafunso 10 Omwe Achinyamata Amadzifunsa
  • Kodi Mfundo Yoti Zamoyo Zinachita Kusanduka ndi Yogwirizana ndi Baibulo?
    Nsanja ya Olonda—2008
Onani Zambiri
Galamukani!—2006
g 9/06 tsamba 1-2

Zamkatimu

September 2006

Magazini Yapadera

Kodi Mlengi Alipo?

Kodi n’zomveka kukhulupirira kuti kuli Mlengi chifukwa cha kupangidwa mwaluso kwa zinthu zamoyo?

Kodi Muyenera Kukhulupirira Ndani? 3

Kodi Zamoyo Zimatiphunzitsa Chiyani? 4

Kodi Mulungu Anagwiritsa Ntchito Chisinthiko Polenga Zamoyo? 9

Kukambirana ndi Katswiri wa Sayansi 11

Pulofesa wina wa sayansi ya zimene zimachitika m’kati mwa zinthu zamoyo akufotokoza maganizo ake pa nkhani ya chisinthiko.

Kodi Chisinthiko Chinachitikadi? 13

Kodi kusintha kwa maselo a zamoyo kapena kupulumuka kwa zamoyo zamphamvu zokhazokha kumayambitsa mitundu yatsopano ya zamoyo?

Kodi Sayansi Imatsutsana ndi Nkhani ya mu Genesis? 18

Kodi Baibulo limaphunzitsadi kuti zinthu zonse zinalengedwa m’masiku sikisi enieni a maola 24?

Chifukwa Chimene Timakhulupirira Kuti Kuli Mlengi 21

Asayansi ndi ochita kafukufuku ena akufotokoza zifukwa zawo.

Dongosolo Lodabwitsa la Zomera 24

Kodi zomera zimapanga mizere yozungulirazungulira pokula, mwangozi chabe?

Kodi Ndingafotokoze Bwanji Zimene Ndimakhulupirira Zokhudza Chilengedwe? 26

Onani mmene wachinyamata angafotokozere zikhulupiriro zake kusukulu.

Kodi Zimene Mumakhulupirira Zili ndi Ntchito? 29

Onani mmene zimakhudzira moyo wanu wonse.

30 Zochitika Padzikoli

31 Kodi Mungayankhe Bwanji?

32 Kodi Mulungu Amatisamaliradi?

[Mawu a Chithunzi patsamba 2]

Dinosaur: © Pat Canova/​Index Stock Imagery

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena