Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 6
  • Pemphero la Mtumiki wa Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Pemphero la Mtumiki wa Mulungu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Pemphero la Mtumiki wa Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Timatumikira Mulungu “Wachifundo Chochuluka”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • ‘Atate Wanu Ndi Wachifundo’
    Nsanja ya Olonda—2007
  • Chitsimikiziro cha Kukhala Ophunzira
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 6

Nyimbo 6

Pemphero la Mtumiki wa Mulungu

Losindikizidwa

(Aefeso 6:18)

1. Atate wa kumwamba, Mfumu,

Dzina lanu litamandidwetu

Chifundo chanu ndi chosatha,

Komanso ndi chodalirika.

Inde n’chodalirika,

Chifundochi n’chosatha.

2. Mtima wathu uthandizeni

Kuti uzikonda choonadi.

Malamulo anu tisunge,

Nkhosa zanuzo tizifune.

Nkhosa zanu tifune,

Malamulo tisunge.

3. M’tipatse nzeru yakumwamba,

M’tidzaze ndi chikondi mumtima

M’tithandize kukonda anthu,

Onse adziwe M’lungu wathu.

Inde akudziweni,

Tiwakondedi anthu.

(Onaninso Sal. 143:10; Yoh. 21:15-17; Yak. 1:5.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena