Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 54
  • Tikhale ndi Chikhulupiriro

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tikhale ndi Chikhulupiriro
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Tikhale Ndi Chikhulupiriro Cholimba
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tiyenera Kukhala ndi Chikhulupiliro
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Muzisonyeza Kuti Mumakhulupirira Malonjezo a Yehova
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
  • “Tiwonjezereni Chikhulupiriro”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 54

Nyimbo 54

Tikhale ndi Chikhulupiriro

Losindikizidwa

(Aheberi 10:38, 39)

1. Kale Mulungu ankalankhula

Kudzera mwa aneneri.

Lero kudzera mwa mwana wake

Akuti ‘lapanitu.’

(KOLASI)

Kodi chikhulupiriro chathu

N’cho’na ndi cha ntchito?

Chikakhala choterocho,

N’chimenedi chimasunga moyo.

2. Ife mokondwa timvera Yesu,

Tilalikira Ufumu.

Ndipo tilankhula mwaufulu,

Sitibisa cho’nadi.

(KOLASI)

Kodi chikhulupiriro chathu

N’cho’na ndi cha ntchito?

Chikakhala choterocho,

N’chimenedi chimasunga moyo.

3. Ndife olimba m’chikhulupiro,

Sitidzabwerera m’mbuyo.

Kaya adani atiukire,

Tidzapezabe moyo.

(KOLASI)

Kodi chikhulupiriro chathu

N’cho’na ndi cha ntchito?

Chikakhala choterocho,

N’chimenedi chimasunga moyo.

(Onaninso Aroma 10:10; Aef. 3:12; Aheb. 11:6; 1 Yoh. 5:4.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena