Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 24
  • Yang’ananibe Pamphotho!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yang’ananibe Pamphotho!
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Yang’ananibe Maso Anu Pamphotho!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Mukhulupirikebe
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Musalole Kuti Chilichonse Chikulepheretseni Kulandira Mphoto
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Yang’ananibe pa Mphoto
    Nsanja ya Olonda—2009
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 24

Nyimbo 24

Yang’ananibe Pamphotho!

Losindikizidwa

(2 Akorinto 4:18)

1. Pomwe akhungu adzaona

Ndipo ogontha adzamvanso,

Pamene madzi adzayenda

Ngakhale muchipululu,

Pomwe wolumala ’dzadumpha,

Abale athu sadzafanso,

Mudzaona madalitsowa

M’kayang’anabe pamphotho.

2. Osalankhula ’dzalankhula,

Okalamba ku unyamata,

Pomwe nthaka idzatulutsa

Zinthu zambiri zabwino,

Pomwe ana ’dzaimba nyimbo,

Kudzakhala mtendere konse,

M’dzaona ’kufa atauka,

M’kayang’anabe pamphotho.

3. Mimbulu idzadya ndi nkhosa,

Zilombo zoopsa ndi ng’ombe.

Mwana adzazitsogolera,

Ndipo zidzamvera iye.

Pamene mantha ndi misozi

Zidzakhala zinthu zakale,

Mudzaona zinthu zonsezi,

M’kayang’anabe pamphotho.

(Onaninso Yes. 11:6-9; 35:5-7; Yoh. 11:24.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena