Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 28
  • Nyimbo Yatsopano

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nyimbo Yatsopano
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Imbani Chitamando cha Yehova Molimbika!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tidzakhala Ndi Moyo Wosatha
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 28

Nyimbo 28

Nyimbo Yatsopano

Losindikizidwa

(Salmo 98)

1. Imbira M’lungu, Imba nyimbo yatsopano;

Unene kwa onse Ntchito zake zonse.

Umutamande, Mulungu ndi wopambana.

Poweruza anthu N’ngwachilungamodi.

(KOLASI)

Imbani!

Nyimbo yatsopano!

Imbani!

Yehova ndi Mfumu.

2. Fu’la mokondwa, Fuula kwa Mfumu yathu!

Mutamandenitu, Ndi nyimbo mokondwa.

Tiyeni tonse Timuimbire mokweza.

Zeze ndi lipenga Ziimbe pamodzi.

(KOLASI)

Imbani!

Nyimbo yatsopano!

Imbani!

Yehova ndi Mfumu.

3. Nyanja ndi zinthu Za momwemo zim’tamande.

Inde chilengedwe Chonse chim’tamande.

Mtunda ukondwe, Mitsinjenso ikondwere.

Mapiri ndi zigwa, Nazo zim’tamande.

(KOLASI)

Imbani!

Nyimbo yatsopano!

Imbani!

Yehova ndi Mfumu.

(Onaninso Sal. 96:1; 149:1; Yes. 42:10.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena