Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 16
  • Thawirani ku Ufumu wa Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Thawirani ku Ufumu wa Mulungu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Thaŵirani ku Ufumu wa Mulungu!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Pitirizanibe Kufunafuna Ufumu Choyamba
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Iri Nditsiku la Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 16

Nyimbo 16

Thawirani ku Ufumu wa Mulungu

Losindikizidwa

(Zefaniya 2:3)

1. Bwerani kwa Yehova ofatsanu,

Zinthu zolungamadi muchite.

Tsiku la Yehova likadzafika

Mwina mungadzabisike.

(KOLASI)

Thawirani ku ’fumu wa M’lungu,

Khalani mbali yake.

N’kumene mudzapeza chitetezo.

M’mvereni, musachedwe.

2. Anjala ya choonadi nonsenu

Mudzamva chisoni mpaka liti?

Bwerani kwa Yehova m’pulumuke

Pansi pa Yesu khalani.

(KOLASI)

Thawirani ku ’fumu wa M’lungu,

Khalani mbali yake.

N’kumene mudzapeza chitetezo.

M’mvereni, musachedwe.

3. Tukulani mitu mosangalala,

Onanitu Ufumu wayamba.

Landirani kuwala kwa Yehova,

Muopeni iye yekha!

(KOLASI)

Thawirani ku ’fumu wa M’lungu,

Khalani mbali yake.

N’kumene mudzapeza chitetezo.

M’mvereni, musachedwe.

(Onaninso Sal. 59:15; Miy. 18:10; 1 Akor. 16:13.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena