Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 18
  • Chikondi cha Mulungu N’chosatha

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chikondi cha Mulungu N’chosatha
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Chikondi Chokhulupirika cha Mulungu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Chikondi cha Mulungu Chokhulupirika
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kodi Timapindula Bwanji ndi Chikondi Chokhulupirika cha Yehova?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • Ndi Mkazi pa Chitsime
    Bukhu Langa la Nkhani za Baibulo
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 18

Nyimbo 18

Chikondi cha Mulungu N’chosatha

Losindikizidwa

(Yesaya 55:1-3)

1. Chikondi cha M’lungu.

Ndithudi ndi chachikulu.

Iye anapereka

Mwana wake kwa ife

Kuti tipeze moyo,

Tipepezenso chimwemwe.

(KOLASI)

Inu nonse aludzu,

Dzamweni kwaulere.

Madzi opatsa moyo;

N’chifundo cha M’lungu.

2. Chikondi cha M’lungu.

Ntchito zake ndi umboni.

Watikonda popatsa

Mwana wake Ufumu

Pokwanitsa pangano.

Ufumu wake wadza.

(KOLASI)

Inu nonse aludzu,

Dzamweni kwaulere.

Madzi opatsa moyo;

N’chifundo cha M’lungu.

3. Chikondi cha M’lungu.

Nafenso tichisonyeze.

Tithandize ofatsa,

Kufuna chilungamo.

Tilalike kwa onse,

Uthenga wotonthoza.

(KOLASI)

Inu nonse aludzu,

Dzamweni kwaulere.

Madzi opatsa moyo;

N’chifundo cha M’lungu.

(Onaninso Sal. 33:5; 57:10; Aef. 1:7.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena