Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 72
  • Tikulalikira Choonadi Chonena za Ufumu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tikulalikira Choonadi Chonena za Ufumu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tilalikire Choonadi cha Ufumu
    Imbirani Yehova
  • Kudziŵitsa Chowonadi Chaufumu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • “Kunyumba ndi Nyumba”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 72

NYIMBO 72

Tikulalikira Choonadi Chonena za Ufumu

Losindikizidwa

(Machitidwe 20:​20, 21)

  1. 1. Poyamba sitinkadziwa

    Zinthu zoti tizichita.

    M’lungu anatipatsa

    Choonadi ndi kuwala

    Ndipo tinazindikira

    Chifuniro cha Yehova,

    Kuti tim’tumikire

    Ndi kumalengeza dzina lake.

    Timalalikira anthu

    Mumakomo ndi mumsewu.

    Timathandiza anzathu

    Kuti adziwe Yehova.

    Tiyeni tiziyesetsa

    Kulalikira mwakhama

    Mpaka pomwe Yehova

    Adzanene kuti tamaliza.

(Onaninso Yos. 9:9; Yes. 24:15; Yoh. 8:​12, 32.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena