Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 95
  • Kuwala Kukuwonjezerekabe

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kuwala Kukuwonjezerekabe
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Kuwala Kukuwonjezereka
    Imbirani Yehova
  • Kuunika Kumkabe Kuuŵala
    Imbirani Yehova Zitamando
  • “Onetsani Kuwala Kwanu”
    Imbirani Yehova
  • N’chifukwa Chiyani a Mboni za Yehova Anasintha Zinthu Zina Zomwe Ankakhulupirira?
    Mafunso Ofunsidwa Kawirikawiri
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 95

NYIMBO 95

Kuwala Kukuwonjezerekabe

Losindikizidwa

(Miyambo 4:18)

  1. 1. Aneneri akale ankafuna

    Kudziwa za Yesu Mesiya.

    Mzimu wa M’lungu unaneneratu

    Kuti adzatipulumutsa.

    Nthawi yakwana akulamulira.

    Umboni wake ulipo.

    Kudziwa zimenezi ndi mwayi

    Waukulu womwe tili nawo.

    (KOLASI)

    Kuwala kwa panjira yathu

    Kukuwonjezerekabe.

    Zomwe M’lungu akuulula

    Zimatitsogoleradi.

  2. 2. Ambuye wathu wasankha kapolo

    Amene akumatidyetsa.

    Kuwala kwa choonadi panopa

    Kukungowonjezerekabe.

    Pano tikuyenda molimba mtima,

    Tikumayenda mowala.

    Tikuthokoza Yehova chifukwa

    Watipatsa choonadichi.

    (KOLASI)

    Kuwala kwa panjira yathu

    Kukuwonjezerekabe.

    Zomwe M’lungu akuulula

    Zimatitsogoleradi.

(Onaninso Aroma 8:22; 1 Akor. 2:10; 1 Pet. 1:12.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena