Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 132
  • Tsopano Ndife Thupi Limodzi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tsopano Ndife Thupi Limodzi
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tsopano Ndife Thupi Limodzi
    Imbirani Yehova
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 132

NYIMBO 132

Tsopano Ndife Thupi Limodzi

Losindikizidwa

(Genesis 2:​23, 24)

  1. 1. Fupa la mafupa anga,

    Ndiwe mnofu wa mnofu wanga.

    M’lungu wandipatsa mnzanga,

    Pano ndiwe wanga

    Ndife thupi limodzidi.

    Tizilandira madalitso.

    Monga mwamuna ndi mkazi

    Pano ndife banja.

    Tizitumikira Yehova.

    Tsiku ndi tsiku

    Tikulitse chikondi.

    Zimene talumbirazi

    Tizichita kwa moyo wonse.

    Tizilemekeza M’lungu

    Ndipo ukhalebe wanga.

(Onaninso Gen. 29:18; Mlal. 4:​9, 10; 1 Akor. 13:8.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena