Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 58
  • Kufufuza Anthu Okonda Mtendere

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kufufuza Anthu Okonda Mtendere
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Kufufuza Anthu Okonda Mtendere
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 58

NYIMBO 58

Kufufuza Anthu Okonda Mtendere

Losindikizidwa

(Luka 10:6)

  1. 1. Yesu anatilamula kuti

    Tiuze anthu uthenga,

    Amve mawu a Yehova.

    Ankakonda nkhosa za Mulungu.

    Ankazifufuza

    Mwakhama tsiku lonse.

    Nyumba ndi nyumba, mumsewu,

    Timauza aliyense

    Kuti posachedwa mavuto atha.

    (KOLASI)

    Tifufuze

    Okonda mtendere m’dzikoli.

    Tifufuze

    Ofuna kupulumutsidwa.

    Tifufuze

    Kulikonse.

  2. 2. Tifufuzebe anthu mwakhama.

    Alipo ambiri

    Omwe tingathe kuwathandiza.

    Poti timawakonda kwambiri,

    Tibwererekonso

    Tikawalimbikitse.

    M’matauni ndi m’midzinso,

    Tikapeza omvetsera

    Timasangalala powaphunzitsa.

    (KOLASI)

    Tifufuze

    Okonda mtendere m’dzikoli.

    Tifufuze

    Ofuna kupulumutsidwa.

    Tifufuze

    Kulikonse.

(Onaninso Yes. 52:7; Mat. 28:​19, 20; Luka 8:1; Aroma 10:10.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena