Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 68
  • Tizifesa Mbewu za Ufumu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tizifesa Mbewu za Ufumu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Fesani Mbewu za Ufumu
    Imbirani Yehova
  • Kufesa Mbewu za Ufumu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kugwirizana kwa Baibulo Lonse
    Baibulo—Kodi Ndilo Mawu a Mulungu Kapena a Munthu?
  • Mbewu ya Njoka—Yavumbulidwa Motani?
    Nsanja ya Olonda—1996
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 68

NYIMBO 68

Tizifesa Mbewu za Ufumu

Losindikizidwa

(Mateyu 13:​4-8)

  1. 1. Bwerani mudzagwire ntchito

    Yotumikira Ambuye.

    Iye adzakuthandizani

    Mukamvera malangizo.

    Mbewu za choonadi zikula

    M’mitima ya omvetsera.

    Choncho tumikirani mwakhama

    Pa ntchito imene mwapatsidwa.

  2. 2. Kuti ntchito iyende bwino

    Zingadalire inuyo.

    Mukaphunzitsa bwino anthu

    Adzakonda choonadi.

    Muziwathandiza kupirira

    Mavuto amudzikoli.

    Mudzasangalala mukaona

    Kuti akukonda choonadi.

(Onaninso Mat. 13:​19-23; 22:37.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena