Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 54
  • Tiyenera Kukhala Oyera

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tiyenera Kukhala Oyera
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Kukhala Woyera Kumatanthauza Chiyani?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
  • “Woyera, Woyera, Woyera Ndi Yehova”
    Yandikirani Yehova
  • “Mukhale Oyera”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • ‘Ine Yehova Mulungu Wanu Ndine Woyera’
    Nsanja ya Olonda—2009
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 54

Nyimbo 54

Tiyenera Kukhala Oyera

(1 Petro 1:15, 16)

1. Mulungu wati tikhale oyera,

Poti Kristu anatiyeretsa.

Monga oyera, odzichepetsa,

Openyerera onse awone.

2. Yehova anatipatula ife,

“Mtundu woyera” ndi “nkhosa zina.”

Tisonyezetu mwa kayendedwe

Kuti timasunga malamulo.

3. Popitabe patsogolo Mulungu

Amatiyenga modabwitsadi.

Apatsa anthu ake cho’nadi,

Choncho ‘tisayang’ane kumbuyo.’

4. Tipeze mipata tikumakula,

M’chiyero, kuyenda m’kuunika.

Tama Yehova, mkondweretseni,

Ali Woyera ndi wolungama.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena