Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 24
  • ‘Sitiri a Dziko Lapansi’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Sitiri a Dziko Lapansi’
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Opulumuka Sayenera Kukhala “Mbali ya Dziko”
    Mtendere Weniweni ndi Chisungiko—Kodi Mungazipeze Motani?
  • Khalani Olimba Mtima!
    Nsanja ya Olonda—1993
  • “Yesu Kristu Ndiye Ambuye”—Motani Ndipo Liti?
    Nsanja ya Olonda—1994
  • ‘Khalani Amphamvu Ndipo Limbikani Mtima’
    Nsanja ya Olonda—2003
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 24

Nyimbo 24

‘Sitiri a Dziko Lapansi’

(Yohane 17:16)

1. M’lungu anatipatula,

Timpatsatu mtima wathu.

Sitiri mbali ya dziko;

Monga Kristu, timasankha.

2. Tipeŵe njira zadziko,

Tichite ntchito ya M’lungu.

Tipeŵe zinthu zathupi

Kuti tikhale ndi moyo.

3. Oyanjana ndi Mulungu,

Adzadedwa ndi dzikoli.

Tiyembekeza chizunzo,

Koma M’lungu ateteza.

4. Chotero timalimbika.

Mbuye anatipemphera:

‘Asamalireni ndithu.’

Ndipo atisamalira.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena