Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 74
  • Yehova, Wopereka Populumukira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova, Wopereka Populumukira
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Amapereka Populumukira
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Yehova Amapereka Chipulumutso
    Imbirani Yehova
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Imbani Chitamando cha Yehova Molimbika!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 74

Nyimbo 74

Yehova, Wopereka Populumukira

(Salmo 18:1, 2)

1. M’tsiku lathu ulosi ukukwanira.

Satanayo wagwa; tsokadi padziko.

Mulungu wakhazika Yesu Mfumu. Tiimba:

‘Ya apulumutsa’ (indedi).

(Korasi)

2. Kukhulupirika kwathu kuyesedwa;

Mzimu wa dzikoli umatiukira.

Kuganiza kukhale koyeradi, tilimbe,

Ndi kupulumuka (o eya).

(Korasi)

3. Yesu adzaphwanya Satana pa Nkhondo,

Kulira ndi imfa sizidzakhalako.

Mmwamba dziko zikhala zatsopano, adziŵa

Tapulumutsidwa (ndithudi).

(KORASI)

Yehova apereka pothaŵira.

Adani azadziŵa kuti Ya ndi Thanthwe.

Molimbika, timtumikire, timtamanda

Yehovayo, Pothaŵirapo, Mtamandeni.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena