Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 153
  • Yehova, Mulungu wa Chipulumutso Chathu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova, Mulungu wa Chipulumutso Chathu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Khalanibe ndi “Chiyembekezo cha Chipulumutso” Choŵala!
    Nsanja ya Olonda—2000
  • Kodi Chipulumutso N’chiyani?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
  • Chipulumutso Zimene Chimatanthauza Kwenikweni
    Nsanja ya Olonda—1997
  • Lino Ndilo Tsiku la Chipulumutso!
    Nsanja ya Olonda—1998
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 153

Nyimbo 153

Yehova, Mulungu wa Chipulumutso Chathu

(Salmo 85:7)

1. Mbuye Yehova wammwamba,

Tikhululukirenitu.

Tinabadwa mu uchimo

Tinalibechowonadi.

Chonde tipulumutseni

Timuke kudziko lanu.

Tiyanjanitsidwe nanu,

Tiimbe chipulumutso.

Tiimbe chipulumutso.

2. Tiri m’khola lanu Mbuye,

Monga nkhosa za Kristuzo.

Chipulumutso tipeza

Ife anthu osokera.

Mtendere mupereka kwa

Wodzichepetsa mitima.

Anzeru akuwopani;

Chipulumutso chafika.

Chipulumutso chafika.

3. Cho’nadicho chimakula!

Tikondwere ndi kufu’la.

Tikuwona zodabwitsa,

Mwana wanu alamula.

Ndiyo nthaŵi ya Ufumu,

Pomwe mtendere ukula.

Tilengeze dziko lonse.

Mwapatsa chipulumutso.

Mwapatsa chipulumutso.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena