Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 86
  • Kukulitsa Chipatso cha Chikondi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kukulitsa Chipatso cha Chikondi
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Tizisonyeza Chikondi
    Imbirani Yehova
  • “Mubale Chipatso Chambiri”
    Nsanja ya Olonda—2003
  • Yehova Amakonda Anthu Amene ‘Amabereka Zipatso’ Mopirira
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
  • ‘Chachikulu cha Izi Ndicho Chikondi’
    Nsanja ya Olonda​—1990
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 86

Nyimbo 86

Kukulitsa Chipatso cha Chikondi

(1 Akorinto 13:8)

1. Mwa chikondi M’lungu apatsa

Kwa atumiki ake onse

Zochitira chifuniro

Chake chopatulikacho.

Ayamikira mzimuwo;

Amakulitsa mphatsozi;

Nasamala kopambana—

Mphatso ija ya chikondi.

2. Modekha tisonyezetunso

Mikhalidwe yautumiki;

Komabe timasumika

Kukwanitsa chofunika.

Ndi maganizo okhatu

Sitingadyetsetu nkhosa;

Tichite ndi mtima wonse

Kupeza nawo dalitso.

3. Tiyeni tisunge mwaphamphu

Chomangira cha mtenderecho.

Tidekhedi povutika;

Ndi kuthandizanso ena.

Ngakhale mu zochepazo

Tipezetu chikondwero;

Kukwaniritsa chikondi

Ndi kufanana ndi M’lungu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena