Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 116
  • ‘Muyenera Kuthandiza Ofookawo’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Muyenera Kuthandiza Ofookawo’
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • “Muthandize Ofookawo”
    Imbirani Yehova
  • “Muzithandiza Ofooka”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • ‘Kondanani Wina ndi Mnzake’
    Nsanja ya Olonda—2003
  • Kodi Mumaona Anthu Ofooka Mmene Yehova Amawaonera?
    Nsanja ya Olonda—2014
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 116

Nyimbo 116

‘Muyenera Kuthandiza Ofookawo’

(Machitidwe 20:35)

1. Zofooka nzambiri

Tiri nazodi.

Koma Yehova ndithu,

Atikondabe.

Iye ngwachifundo,

Timuyamikira.

Titsanze chikondicho,

Thandiza ena.

2. M’malo mwa kusuliza,

Tikumbukire

Ubwino upezedwa

Mwachifundocho.

Tikhale achangu,

Kuwalimbikitsa.

Powapatsa thandizo,

Atonthozedwa.

3. ‘Ndani wofo’ka nane?’

Ati Paulo.

Tilingalire ena,

Timve chisoni.

Kwa ’mphamvu tinena:

‘Mthandize ofo’ka.’

Anagudwa ndi Kristu,

Kupeza moyo.

4. Tithandize ofo’ka,

Ya amveketsa.

Powathandiza zedi,

Tidzadaladi.

Ali a Mulungu.

Akhale amphamvu.

Tikawathandizadi,

Tidzalimba nji.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena