Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 199
  • “Mawonekedwe a Dziko Lino Akusintha”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Mawonekedwe a Dziko Lino Akusintha”
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Zochitika za Padzikoli Zikusintha
    Imbirani Yehova
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Lonjezo la Mulungu la Paradaiso
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 199

Nyimbo 199

“Mawonekedwe a Dziko Lino Akusintha”

(1 Akorinto 7:31, NW)

1. Chinkana akuwononga,

Chilengedwe cha Mulungu,

Tikuyembekezerabe

Kutha kwa kuipaku (kwa dzikoli).

(Korasi)

2. Adaniwo azomola.

Afuna kuchotsa mphamvu.

Tiomba m’manja mokondwa;

Chilakiko nchathudi. (zowonadi)

(Korasi)

3. Mdaniyo adziwonetsa

Nayesa kudodometsa,

Timamatira Mawuwo

Ndi kukhala oyera. (tikhaledi)

(Korasi)

4. Dongosolo lino litha;

Satana adzamangidwa.

Tilalikire mbiriyo

—Ya amatithandiza. (mwachikondi)

(KORASi)

Chinkana dzikoli likusintha,

M’lungu wathu wachifundo

Watikonzera zonse.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena