Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 188
  • Mphatso ya Pemphero

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mphatso ya Pemphero
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Yesu Atiphunzitsa Ife Kupemphera
    Kumamumvetsera Mphunzitsi Wamkuru’yo
  • Pemphero Lingakuthandizeni Kuti Mulungu Akhale Mnzanu
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
  • Tili Ndi Mwayi Wopemphera kwa Mulungu
    Zimene Baibulo Limaphunzitsa
  • Kuyandikira kwa Mulungu m’Pemphero
    Kodi Mulungu Amafunanji kwa Ife?
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 188

Nyimbo 188

Mphatso ya Pemphero

(1 Timoteo 2:8)

1. Ya amva mapemphero

A onse omumvera.

Mwa Yesu Kristu yekha

Tingafike mpandowo.

2. Mapemphero ofika

Ya akhale owona.

Ochokera mumtima

Alemekeza M’lungu.

3. Popemphera kwa M’lungu

Tiyeni tidzipende,

Tisabwereze mawu,

Komatu mwachikondi.

4. Tipemphe nthaŵi zonse

Poyenda munjirayi.

Pemphero litonthoza;

Ndimphatso ya Mulungu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena