Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 198
  • Kufika Pakudziŵa Mulungu Wathu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kufika Pakudziŵa Mulungu Wathu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Tipange Mbiri Yabwino kwa Mulungu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tipange Dzina Labwino kwa Mulungu
    Imbirani Yehova
  • Yehova Mulungu Wamkulu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Achimwemwe, Ngachifundo!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 198

Nyimbo 198

Kufika Pakudziŵa Mulungu Wathu

(Yohane 17:3)

1. Ndithu tidziŵa, Mmene M’lungu,

amveradi.

Watimasula Mwachisomo

Ali nafe.

2. Ndi wachifundo Ndi chikondi,

Tizidziŵa.

Timudalira; Ndife fumbi,

Ngwachifundo.

3. Tiphunziratu, Zambiridi,

Za Mulungu.

Tiyesayesa Kuyendabe

Mwa Kristuyo.

4. Titsanziretu Chikondicho,

M’ntchito zathu.

Tidziŵikitse Dzina la Ya,

Ngwowonadi.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena