Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 182
  • “Mvunguti mu Gileadi”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Mvunguti mu Gileadi”
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Mafuta a Basamu wa ku Gileadi Ndi Ochiritsa
    Nsanja ya Olonda—2010
  • Tonthozani Amene ali ndi Chisoni
    Nsanja ya Olonda—2003
  • Khulupirirani Yehova, “Mulungu Amene Amatitonthoza M’njira Iliyonse”
    Nsanja ya Olonda—2011
  • ‘Tonthozani Anthu Onse Olira’
    Nsanja ya Olonda—2011
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 182

Nyimbo 182

“Mvunguti mu Gileadi”

(Yeremiya 8:22)

1. Tamva kuti m’Gileadi;

Mulidi mvunguti.

Utonthoza opsinjika

Uchotsa chisoni.

Umatsitsimutsa ngati

Tiritu otopa,

Nkana okondedwa athu

Agona mu imfa.

2. “Mulungu ndiye chikondi,”

Ndiwamphamvu yonse.

Zimene amatumiza

Zitipindulitsa.

Pitaninso kwa Mulungu

Pemphani kwa iye,

Musabise chirichonse;

Muuzeni zonse.

3. Kumbukirani zinthuzo,

Zochitika kale,

Zinalembedwa kuti ’fe,

Titonthozedwetu.

Landirani chithangato

Modzichepetsatu,

Chidzakuthandizanidi

Kuti mupilire.

4. Kodi mwalingalirapo,

Opsinjika ena?

Kuti enanso ambiri

Ali kuyesedwa?

Muwatonthozetu iwo

Kuti akondwere.

Mukatero mudzadziŵa

Mphamvu ya mvunguti.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena