Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 82
  • Akazi Ali Gulu Lankhondo Lalikulu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Akazi Ali Gulu Lankhondo Lalikulu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • ‘Akazi Amene Agwiritsa Ntchito mwa Ambuye’
    Nsanja ya Olonda—1991
  • Akazi Amathandiza Pokwaniritsa Cholinga cha Yehova
    Nsanja ya Olonda—2014
  • Akazi Okhulupirika Ndiponso Alongo Achikhristu
    Imbirani Yehova
  • Muzilimbikitsa Alongo Mumpingo
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2020
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 82

Nyimbo 82

Akazi Ali Gulu Lankhondo Lalikulu

(Salmo 68:11)

1. Yehova apereka mawu.

Akazi olalikawo

Aumba gulu la umboni;

Afuna kufika athu.

Ayenera kuyamba msanga,

Nasamala mwininyumba.

Mwa kukhala okonzekera,

Agaŵana muntchitoyo.

2. Antchito anzathu alongo,

Tiwapemphera dalitso.

Akwaniritsa kulalika,

Ifenso tiwatamanda.

Koma ambiri ngamasiye,

Onse ali ndi zovuta.

Samalephera misonkhano;

Asonyeza chipiliro.

3. Tiyeni tiwasamalire

Amayi ana akazi.

Amagaŵana mukututa,

Kuyesa kupulumutsa.

Gululi nloyenereradi.

Zochita zake nzaphindu.

Asamalirenidi bwino.

Mawu a Ya ndi owona.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena