Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 177
  • Kodi Tiyenera Kukhala Mtundu Wanji wa Anthu?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Tiyenera Kukhala Mtundu Wanji wa Anthu?
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kulemekeza Atate Wathu Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tamani Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kuyamikira Chifundo cha Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kupeza Ubwenzi wa Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 177

Nyimbo 177

Kodi Tiyenera Kukhala Mtundu Wanji wa Anthu?

(2 Petro 3:11)

1. Tikumbukire tsiku lalikulu la Ya.

Mtima wathu uli kwa iye ndi Mwanayo.

Usiku wapita tsiku liyamba;

Zinthu za Satana zichoka msanga.

Pemphero nlabwino kuti tikhale maso.

Pemphero liri lofunika kwakukulu.

Mwakupempha M’lungu ndi mtima wonsewo,

Tidzapeza mtendere umene atipatsa.

2. Chimwemwe ndi mtendere wathu sizimatha.

Tiri chiwonetso kuti anthu adziŵe.

Kodi tingakhale anthu otani?

Kodi tisonyeze ntchito zotani?

Tifuna kuuza ena za Ufumuwo

Ndi kunena za malonjezo atsopano

Ndi kuti kudzakhaladi chilungamo.

Tipitirizebe kulalikira mbiriyi.

3. Tisamale machitidwe athu a moyo

Mogwirizana ndi malamulo a phindu.

Yesu anatiyeretsa mu’chimo,

Tikondwa ndi mtendere wa Mulungu.

Tikufunabe kukhala opanda banga;

Monga atumiki a Ya ndifedi mfulu.

Tikakhala naye monga Bwenzi lathu,

Adzatithandiza kufikira kumapeto.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena