Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 193
  • Lalikirani “Mbiri Yabwino Imeneyi Yaufumu”!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Lalikirani “Mbiri Yabwino Imeneyi Yaufumu”!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • “Uthenga Wabwino”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Pitirizanibe Kufunafuna Ufumu Choyamba
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 193

Nyimbo 193

Lalikirani “Mbiri Yabwino Imeneyi Yaufumu”!

(Mateyu 24:14, NW)

1. Mbiri yabwinoyi Yaufumu lero

Ilengezedwe m’dziko lonse.

Ndipo dzina labwinolo la Yehova,

Lilemekezedwe ponsepo.

(Korasi)

2. Masiku ngoipa; tiombole nthaŵi

Kuzosangalatsa zadziko.

Ufumu ukhale woyamba mumoyo,

Tipezedi chuma chosatha.

(Korasi)

3. Polalika mbiriyo musawopsedwe,

Nkanatu muli ndi chitsutso.

Mwachifundo pilirani osawopa;

Khalani owona muntchito.

(KORASi)

Lalikirani ponsepo.

Kuti ena adziŵe M’lungu.

Ndipo thandizani onse aitane

pa Ya nayeretse dzinalo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena