Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 216
  • ‘Khalani ndi Chikondi Chenicheni’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Khalani ndi Chikondi Chenicheni’
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • “Mukondane ndi Chikondi Chaubale”
    Nsanja ya Olonda—2004
  • Pitirizani Kusonyezana Chikondi Chenicheni
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • Kupeza Mfungulo ya Chikondi cha pa Abale
    Nsanja ya Olonda—1993
  • Kodi Mungasonyeze Bwanji Kuti Mumakonda Mwamuna Kapena Mkazi Wanu?
    Mfundo Zothandiza Mabanja
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 216

Nyimbo 216

‘Khalani ndi Chikondi Chenicheni’

(Aroma 12:10)

1. Ndichikondi chotani Yehova wasonya

Kwa akumfunafuna!

Chifundo ukoma zibweretsa chimwemwe;

Mwa iye tiri ndi mpumulo.

2. Tichitirane chifundocho chaubale

Potumikira M’lungu.

Tisonyeze khalidwe labwino kwambiri

Mwa mtenderedi muumodzi.

3. Popeza ndife Akristu tiri amodzi,

Chikondicho chikule.

Tipatse ulemu abale athu onse

Tisawakhumudwitse ndithu.

4. Tipereke chisamaliro kuchikondi,

Yesu anaphunzitsa.

Ukoma wa mtima ndi kudziŵa chikondi

Kumatidzetsera chimwemwe.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena