Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 120
  • Khalani Okhazikika Monga Rute

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Khalani Okhazikika Monga Rute
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • “Kumene Inu Mupite Inenso Ndipita Komweko”
    Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo
  • “Kumene Inu Mupite Inenso Ndipita Komweko”
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Mfundo Zazikulu za M’buku la Rute
    Nsanja ya Olonda—2005
  • Anali “Mkazi Wabwino Kwambiri”
    Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 120

Nyimbo 120

Khalani Okhazikika Monga Rute

(Rute 1:15-17)

1. Naomi ati Rute pita,

Nkana sizimukondweretsa.

Rute akana kubwerera,

Mtima’ke uli pa Naomi.

2. ‘Ayi sindidzakusiyani.

Komwe mukhala ndidzakhala.

Komwe mugona ndidzagona.

Komwe mufera ndidzafera.

3. ‘Anthu anu ndianthu anga,

M’lungu wanu ndi M’lungu wanga.

Mulungu awonjezerepo

Ngati ine ndisiya inu.’

4. Rute anaika chitsanzo!

Pakusonyeza chikonditu.

Tisonyeze kukhazikika.

Timamatire kwa Mulungu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena