Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 126
  • Kulengeza Chowonadi Chaufumu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kulengeza Chowonadi Chaufumu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Ufumu wa Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova
  • Imbani Nyimbo ya Chisangalalo Chaufumu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kuyenda m’Dzina la Mulungu Wathu
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 126

Nyimbo 126

Kulengeza Chowonadi Chaufumu

(Mateyu 10:7)

1. Chowonadi ndichapatali;

Onga nkhosa asangalala.

Mofulumira tilalike,

Ndithudi, Ufumuwo wadza.

2. Kunyumba ndi nyumba tipita;

Tifuna kubzala cho’nadi.

Tiri ndi thandizo la M’lungu.

Mzimuwo utipatsa mphamvu.

3. Tadalitsidwa ndi ntchitoyo.

Tiyeni tiyeseyesetse,

Kudzetsa chiyembekezocho.

Cho’nadi chidzawapumitsa.

4. Tilengeze m’dziko lonseli

Kuti Yesu alamulira.

Ufumuwo udzadziŵitsa

Za dzina la Yehova Mfumu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena