Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 200
  • Chitsimikiziro cha Kukhala Ophunzira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chitsimikiziro cha Kukhala Ophunzira
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Chikondi Ndi Khalidwe Lamtengo Wapatali Kwambiri
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Kulani M’chikondi
    Nsanja ya Olonda—2001
  • “Pitirizani Kusonyeza Chikondi”
    Yandikirani Yehova
  • “Mulungu Ndiye Chikondi”
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 200

Nyimbo 200

Chitsimikiziro cha Kukhala Ophunzira

(Yohane 13:34, 35)

1. M’kusonyeza chikondi,

Akristu adziŵika.

Kristu anasonyeza

Chikondi namveratu.

Chingapezeke kuti

Chikondi choterechi?

Yense ataya moyo,

Kupatsa wina moyo.

2. Chikondi chowonacho,

Chiri cha kwa onsewo.

Nchaukoma wambiri,

Chimadalitsa ena.

Ndilamulo la Yesu;

Chikondi chithandiza,

Sichidzipindulira,

Chimathandiza ena.

3. Chimawona zabwino.

Chimangira ubale.

Chikondi kwa olakwa

Chifunira ubwino.

Dziko lidzatidziŵa

Mwa chikondi chathucho,

Mwa Mwana wa mmwambayo.

O “Mulungu nchikondi”!

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena