Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 28
  • Dalitsani Kusonkhana Kwathu Pamodzi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Dalitsani Kusonkhana Kwathu Pamodzi
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Dalitsani Msonkhano Wathu!
    Imbirani Yehova
  • Mudalitse Msonkhano Wathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kuyamikira Kudekha kwa Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Bwerani kwa Mulungu Kuti Mupulumuke
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 28

Nyimbo 28

Dalitsani Kusonkhana Kwathu Pamodzi

(Ahebri 10:24, 25)

1. M’tidalitse posonkhana,

Kulambira inu, Ya.

Tiyamika malo ano;

Mzimu ukhale nafe.

2. Tisoŵatu mwauzimu;

Mutidzaze n’cho’nadi.

M’tiphunzitse kulalika,

Mutidzaze chikondi.

3. Pamsonkhano wokomawu;

Tifune chilungamo.

Kutitu tidziŵe inu

Tikhalebe ofatsa.

4. Mudalitse misonkhano;

Mtendere ndi umodzi.

Mu’tumiki Waufumu,

Titametu Ufumu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena