Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 5
  • Chilengedwe Chonse, Tamandani Yehova!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chilengedwe Chonse, Tamandani Yehova!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Yehova Mulungu Wathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Loŵani m’Mabwalo a Kachisi wa Yehova!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Opatulidwa Kukhala Atamandi Achimwemwe pa Dziko Lonse
    Nsanja ya Olonda—1997
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 5

Nyimbo 5

Chilengedwe Chonse, Tamandani Yehova!

(Salmo 148)

1. Chilengedwe, tamani Ya;

Mdalitse dzina lake.

Tsiku lonse angelonso

Amtamanda mokondwa.

2. Dzuŵa mwezi ndi nyenyezi

Zidziŵitsa Mulungu.

Zimamvera malamulo; Sizidzachoka konse.

3. Dziko limtamanda iye.

‘Nkhosazo’ zikusankha.

Kutumikira Mulungu Mumabwalo mokondwa.

4. Khamu lalikulu lidze

Kukachisi wa M’lungu.

Tiyenera kumlambira. Yekhayo ngwokwezeka.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena