Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 7
  • Chiyembekezo cha Mpumulo wa Anthu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chiyembekezo cha Mpumulo wa Anthu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Anakonza Zoti Tikhale ndi Ufulu
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
  • Chaka Choliza Lipenga cha Yehova—Nthawi Yathu Yakusangalala
    Nsanja ya Olonda—1987
  • Mafunso Ochokera kwa Oŵerenga
    Nsanja ya Olonda—2004
  • Chaka Choliza Lipenga cha Akristu Chifika Pachimake mu Zaka Chikwi
    Nsanja ya Olonda—1987
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 7

Nyimbo 7

Chiyembekezo cha Mpumulo wa Anthu

(Levitiko 25:10)

1. Chilengedwe chibuula.

Mosaphula kanthu.

Koma Sabata lafika.

Mpumulo wafika.

2. Chimasuko cha mtendere,

Kumasula zonse,

Kristu azadzibweretsa;

M’lungu am’lamula.

3. Mu’lamuliro wa Kristu,

Zonse zikonzedwa.

Chimasuko chidzathetsa

Ukapolo wonse.

4. Anthu a Ya abukitsa

Chiyembekezochi.

Nalindira kuyankhidwa

Kwa mapempho awo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena