Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 215
  • Kusonyeza Chifundo kwa Ena

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kusonyeza Chifundo kwa Ena
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • ‘Atate Wanu Ndi Wachifundo’
    Nsanja ya Olonda—2007
  • Timatumikira Mulungu “Wachifundo Chochuluka”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • Kodi Tingasonyeze Bwanji Chifundo?
    Nsanja ya Olonda—2007
  • Anthu Achifundo Amakhala Odala
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 215

Nyimbo 215

Kusonyeza Chifundo kwa Ena

(Luka 6:36)

1. Polamula za chigumulacho

Kuwononga anthu akale,

Yehova anati kwa Nowayo:

‘Umange lalika adziŵe!’

Kodi Nowa ananyala nyaza

Kumangatu chingalaŵacho?

Ayi, mwachifundo cha Mulungu,

Anamanga nalalikabe.

2. Dongosolo lakale likutha,

Mwachifundo M’lungu wanena

Kuti mbiriyo iperekedwe,

Kuti yense wofuna amve.

Kodi mwati: “Sindingala like;

Ndiri wosadziŵa kunena”?

Ngati mwalandirapo chifundo,

Mzimu udzakuthandizani.

3. Chisangalalo chikupezeka

Mwachowonadi ndi chifundo.

Kulaŵa za Ufumu wa M’lungu

Kuchoka m’dzanja la Yehova!

Tisonyeze chifundo kwa ena

Mwa kulimbitsa anthu onse:

Pangani kudzipereka msanga;

Ku Ufumu wa Mulunguwo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena