Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 3
  • Kugonjetsa Dziko

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kugonjetsa Dziko
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Nyimbo Yachilakiko
    Imbirani Yehova Zitamando
  • ‘Chitani Monga Amuna’
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tikuyamikani, Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kulemekeza Atate Wathu Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 3

Nyimbo 3

Kugonjetsa Dziko

(Yohane 16:33)

1. Pamene timka tilaka

Mumphamvu ya Yehova,

Amachititsa kulaka

Munkhondo yolungama.

Timakwiyitsa mitundu

Mwa kufalitsa kwathu.

Modalira chilakiko,

Tidzamuka moguba.

2. M’dzikoli tidzavutika.

Tidziŵa zimenezo.

Yesu anati “Limbani!”

‘Ndidzakusunganibe.’

Tingapeze chilakiko,

Poti nkhondo siyathu.

Mulungu achita nkhondo;

Moto upha adani.

3. Tililaka dziko lino

Mokhulupira Kristu.

Popeza Ufumu wadza,

Amaponya lupanga.

Monga analaka dziko,

Ife tingateronso.

Modalira M’lungu wathu,

Tidzagonjetsa zedi.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena