Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 123
  • Pitani Patsogolo!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Pitani Patsogolo!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Pitani Patsogolo
    Imbirani Yehova
  • Pita Patsogolo
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • “Kunyumba ndi Nyumba”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • “Muzionetsa Kuwala Kwanu”
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 123

Nyimbo 123

Pitani Patsogolo!

(Ahebri 6:1)

1. Pita patsogolo ku’chikulire!

Mulungu afuna kuti tipeze luso.

Yesetsa kuwongola utumiki,

M’lungu adalitsa ntchito.

Pali malo antchito kwa onse;

Nditchito Yesu anachitayo.

Yang’anani kwa M’lungu kuti m’sagwe.

Imirani chilungamo.

2. Pita patsogolo kulalikira!

Lengeza mbiri yabwino kwa anthu onse.

Tamandani Yehova Mfumu yathu

Mwa kuchitira umboni.

Nkana oipa akuwopseni,

Musabwevukeko amve onse

Ufumu wa Yehova wayandika.

Lengezani chowonadi.

3. Pita patsogolo; Wongoleranso

Luso pali ntchito yambiri yochitapo!

Mzimu wa M’lungu udzakuthandiza

Kuti upeze chimwemwe.

Kondani abale anu onse;

Chifukwa cha dzina la Mulungu.

Athandize kupita patsogolo,

Kuŵalitsa kuunika.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena