Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 129
  • Tsopano Ndiyo Nthaŵi!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tsopano Ndiyo Nthaŵi!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mudzasungabe Umphumphu?
    Nsanja ya Olonda—2008
  • N’chifukwa Chiyani Muyenera Kusunga Umphumphu?
    Nsanja ya Olonda—2008
  • Pitirizani Kukhala ndi Mtima Wosagawanika
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
  • Yendani mu Umphumphu
    Nsanja ya Olonda—2004
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 129

Nyimbo 129

Tsopano Ndiyo Nthaŵi!

(Marko 13:10)

1. Tsono tilaliketu,

Chowonadi chimveke.

Musakhale ndi mantha;

Sonyeza Ufumu wa M’lungu.

Tichenjezetu anthu onse.

Kuti athawe mu Babulo

Kupulumuka imfa yake.

Awonetse changu pa M’lungu.

Ndinthaŵi tiwonetse changu.

2. Sonyezani kuwona

M’kusonyeza chikondi,

Kuthandiza abale,

Tingachuluke tingachepe.

Titumikiretu Mulungu,

Ndi kukonda cho’nadi chake,

Tiwone chiyanjo chakecho

Ndi kusunga umphumphu wonse.

Ndinthaŵi yosunga umphumphu.

3. Nkhondo idzamenyedwa,

Cho’nadi chidzalaka.

Mdima udzatha psiti.

Tikhale miyuni yoŵala.

Akufa onse adzauka,

Adzadyadi Mkate Wamoyo.

Sitidzawopanso zoipa.

Zonsezi Yehova wanena.

Ndinthaŵi tinene mawuwo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena