Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 41
  • Tamandani Yehova, Thanthwe

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tamandani Yehova, Thanthwe
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Chilengedwe Chivumbula Ulemelero wa Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tiyeni Tonse Titamande Ya
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Ya
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tamani Yehova Mulungu Wathu!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 41

Nyimbo 41

Tamandani Yehova, Thanthwe

(Deuteronomo 32:4)

1. ‘Imvani m’yamba; Ndinene, dziko.

Imvani mawu nonse ofatsa.

Kuphunzitsa kwanga kudzanga mame,

Chowonadi changa chidzanga mvumbi.’

2. O tilengeze Dzina la M’lungu,

Anthu adziŵe kutchuka kwake.

Ndi owetedwa atamande Thanthwe.

Ntchito zake zonse nzachilungamo.

3. Mulungu wathu; ndiwolungama.

Njirazo zake zonse nchikondi.

Ali wolungama ndi wa cho’nadi,

Yehova ali wokhulupirika.

4. Tiwope M’lungu pochita bwino;

Tikondwere ndi malamulowo.

Tisawonongetu mbali yathuyo,

Koma kutumikirabe Yehova.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena