Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 137
  • Nthaŵi Zoikidwiratu Ziyandikira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nthaŵi Zoikidwiratu Ziyandikira
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kulambira Yehova Ambuye Mfumu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Pemphero la Chiyamiko
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kuyenda m’Dzina la Mulungu Wathu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Ufumu wa Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 137

Nyimbo 137

Nthaŵi Zoikidwiratu Ziyandikira

(Habakuku 2:3)

1. O Yehova, Woyera,

Thanthwe lakalelo,

Mu Ziyoni m’bangula;

Chiweruzo chidza.

Ngakhale chikachedwa,

Tidziŵa chidzabe.

Ona mapeto afika;

Tiyembekezera.

2. Mudzadzetsa lupanga

Lanu mosachedwa.

Tikuwona tsopano,

Kulambira kwadza.

Oipawo anyada

Navulaza ife,

Koma nthaŵiyo yafika

Yoti mulamule.

3. Mbuye Mfumu, Yehova,

Ndilo dzina lanu.

Anthu akhale chete

Adziŵe za inu.

Mulamula mwa Yesu

Munjira yamphamvu.

Wokhala pampando, O Ya,

Mulamula dziko.

4. Tifuula mokondwa;

Ndi kuimbira Ya.

Mudzetsa ndi Kristuyo

Chipulumutsocho.

O Wamkulu Wammwamba,

Ndinthaŵi yanudi.

Chotero tiyembekeza

Chilakiko chanu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena