Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 32
  • “Kumka Kunyumba ndi Nyumba”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Kumka Kunyumba ndi Nyumba”
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • “Kunyumba Ndi Nyumba”
    Imbirani Yehova
  • “Kunyumba ndi Nyumba”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • N’chifukwa chiyani a Mboni za Yehova amalalikira kunyumba ndi nyumba?
    Mafunso Ofunsidwa Kawirikawiri
  • Tikulalikira Choonadi Chonena za Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 32

Nyimbo 32

“Kumka Kunyumba ndi Nyumba”

(Machitidwe 20:20)

1. Kumka kunyumba ndi nyumba,

Tilalika Mawu.

Mumidzi ndi mumindanso,

“Nkhosa” zidyetsedwa.

Mbiri Yaufumuyitu,

Yesu ananena,

Ikulalikidwa m’dziko

Ndi am’sinkhu yonse.

2. Tilalike chilanditso,

Kunyumba ndi nyumba.

Chodza kwa oitanira

Dzina la Yehova.

Adzaitana motani

dzina Salidziŵa?

Chotero Dzina Loyera

Limke kunyumbazo.

3. Sikhomo lonse tipeza

Khutu lomvetsera;

Nthaŵi zina tinyozedwa

Ndi okana kumva.

Zinateronso kwa Yesu;

Onse sanamvera.

“Nkhosa” zimva mawu ake;

Ife sitileka.

4. Timke kukhomo ndi khomo

Kulalika mbiri.

Anthu asankhe kukhala

“Nkhosa” pena “mbuzi.”

Tidzatchula dzina Lake,

Ndi cho’nadi Chake.

Popita pamakomowo,

Tidzapeza “nkhosa.”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena