Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 29
  • Tiyeni, Mboninu!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tiyeni, Mboninu!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Pitani Patsogolo Mboninu!
    Imbirani Yehova
  • Pitani Patsogolo Mboninu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Patsogolo, Inu Aminisitala Aufumu!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 29

Nyimbo 29

Tiyeni, Mboninu!

(Luka 16:16)

1. Olimba munthaŵi yamapetoyi,

Ali atumiki oimira mbiri.

Ngakhale Satana atsutsa,

Mwamphamvu ya M’lungu sawopa.

(Korasi)

2. Anthu akana chowonadi ichi.

Otsutsa aletsa dzina la Yehova.

Abwezedwe kumalo awo

Ndi Akristu olimba mtima.

(Korasi)

3. As’kali a Ya safuna zofeŵa.

Sakondweretsa dziko pena mafumu;

Amakhala opanda banga,

Ndiosunga umphumphu wawo.

(KORASi)

Tiyenitu Mboninu, molimba mtima!

Sangalalani muntchito ya Mulungu!

Nenani za Dziko latsopanolo,

Mmene mudzakhala madalitso!

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena