Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 30
  • “Achangu Pantchito Zokoma”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Achangu Pantchito Zokoma”
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Changu Kaamba ka Nyumba ya Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 30

Nyimbo 30

“Achangu Pantchito Zokoma”

(Tito 2:14)

1. Tikhale achangu pazabwino

Polalikira za Ufumu.

Tidziŵa Yehovayo ngwa Nsanje.

Tidzakhalabe m’nyumba yake.

2. Chikondi chikhaletu chowona,

Pomatumikira abale.

Poyandikana ndi Armagedo,

Tisachoke muutumiki.

3. Changu, chikhulupiro, chikondi.

Izi ziri ndi mbali zake.

Kufunitsa kumakhutiritsa,

Ngati moto mumtima mwathu.

4. Tikhale olimba m’masautso,

Chikondi chathu chisazime.

Changu cha kuyeretsa dzina la

Mulungu chitisonkhezera.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena